{"product_id":"durie-mark-mamasulidwe-a-kwa-omangidwa-liberty-to-the-captives-9781923067172","title":"Mamasulidwe a kwa Omangidwa (Liberty to the Captives)","description":"Buku la Mamasulidwa a kwa Omangidwa limapereka zinthu zapadera zoperekera machiritso ndi ufulu. Limapereka makiyi ogwiritsira ntchito mphamvu ya mtanda kutenga 'ufulu wa ulemerero wa ana a Mulungu' (Aroma 8:21 ). Mapemphero ndi zolengeza mu masamba awa zayesedwa m'makontinenti asanu ndi limodzi. Zatsimikizira kuthekera kothandiza kumasula anthu, kuswa linga la mibadwo ndi kuwamasula kukhala mboni zolimba mtima ndi zogwira mtima za mphamvu yopulumutsa ya Khristu.","brand":"Deror Books","offers":[{"title":"Default Title","offer_id":53808127344982,"sku":null,"price":0.0,"currency_code":"EUR","in_stock":false}],"thumbnail_url":"\/\/cdn.shopify.com\/s\/files\/1\/0925\/5829\/5382\/files\/product_image_9781923067172_1_456f4c47-b6ab-4bc3-8a8f-2c90725e1ccb.jpg?v=1783393329","url":"https:\/\/www.momoxbooks.com\/products\/durie-mark-mamasulidwe-a-kwa-omangidwa-liberty-to-the-captives-9781923067172","provider":"momoxbooks","version":"1.0","type":"link"}